Elon Musk wavulidwa

Dec 28, 2025
Friends of Mtonda donate uniforms to needy students

Zimbabwe News Update

🇿🇼 Published: 28 December 2025
📘 Source: Malawi 24

Mpondamatiki Elon Musk, yemweso ndi mwini wa tsamba la mchezo la X lija linkachulidwa kuti Twitter, akusambwadzidwa ndi mai wina yemwe anamubelekera mwana koma sakumuthandiza.

Mayiyu yemwe dzina lake ndi Claire Boucher koma amadziwika bwino ndi dzina loti Grimes, walemba pa tsamba la X kumusambitsa chokweza Musk kamba kosathandiza mwana wawo.

Grimes wati wakhala akumuuza Musk kuti athandize mwana wawoyu yemwe pano akudwala, koma bambo wapakhomo pa mwana alirenjiyu sakuchita kanthu zomwe zamupangitsa mayiyu kuvula chinyawu.

Malawi24

Musk ndi mpondamatiki ku America ndipo wakwanitsa kukhala nawo muboma la Donald Trump kamba ka kakukhupuka kwake. Malipoti akusonyeza kuti Musk ndi bambo wosalora siketi idutse. Malingana ndi tsamba la ‘The Standard’, Musk wafesa ana khumi ndi awiri; indee kukwanilitsa malemba.

Is this news of interest to Malawians?

Elon Musk
📖 Continue Reading
This is a preview of the full article. To read the complete story, click the button below.

Read Full Article on Malawi 24

AllZimNews aggregates content from various trusted sources to keep you informed.

📰 Article Attribution
Originally published by Malawi 24 • December 28, 2025

Powered by
AllZimNews

By Hope